Лагатып YouVersion
БібліяПланы чытанняВідэа
Атрымаць прыкладанне
Выбар мовы
Значок пошуку

Папулярныя біблейскія вершы з GENESIS 2

1

GENESIS 2:24

Buku Lopatulika

BLP-2018

Chifukwa chotero mwamuna adzasiya atate wake ndi amake nadzadziphatika kwa mkazi wake: ndipo adzakhala thupi limodzi.

Параўнаць

Даследуйце GENESIS 2:24

2

GENESIS 2:18

Buku Lopatulika

BLP-2018

Yehova Mulungu ndipo anati, Si kwabwino kuti munthu akhale yekha; ndidzampangira womthangatira iye.

Параўнаць

Даследуйце GENESIS 2:18

3

GENESIS 2:7

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Yehova Mulungu anaumba munthu ndi dothi lapansi, nauzira mpweya wa moyo m'mphuno mwake; munthuyo nakhala wamoyo.

Параўнаць

Даследуйце GENESIS 2:7

4

GENESIS 2:23

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo anati Adamu, Uyu tsopano ndiye fupa la mafupa anga, ndi mnofu wa mnofu wanga; ndipo adzatchedwa Mkazi, chifukwa anamtenga mwa mwamuna.

Параўнаць

Даследуйце GENESIS 2:23

5

GENESIS 2:3

Buku Lopatulika

BLP-2018

Mulungu ndipo anadalitsa tsiku lachisanu ndi chiwiri, naliyeretsa limenelo: chifukwa limenelo adapuma ku ntchito yake yonse imene Mulungu anailenga ndi kupanga.

Параўнаць

Даследуйце GENESIS 2:3

6

GENESIS 2:25

Buku Lopatulika

BLP-2018

Onse awiri ndipo anali amaliseche, mwamuna ndi mkazi wake, ndipo analibe manyazi.

Параўнаць

Даследуйце GENESIS 2:25

Папярэдні разьдзел
Наступны разьдзел
YouVersion

Заахвочваем і заклікаем вас кожны дзень шукаць блізкасці з Богам.

Служэнне

Пра дадатак

Кар'ера

Валянтэрства

Блёг

Прэса

Карысныя спасылкі

Дапамога

Ахвяраваць

Пераклады

Аўдыё Бібліі

Мовы Бібліі

Верш дня


Лічбавае служэнне

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Палітыка прыватнасьціУмовы карыстаньня
Праграма раскрыцця ўразлівасцяў
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Стужка

Біблія

Планы чытання

Відэа