Лагатып YouVersion
БібліяПланы чытанняВідэа
Атрымаць прыкладанне
Выбар мовы
Значок пошуку

Папулярныя біблейскія вершы з GENESIS 7

1

GENESIS 7:1

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo anati Yehova kwa Nowa, Talowani, iwe ndi akunyumba ako onse m'chingalawamo; chifukwa ndakuona iwe kuti uli wolungama pamaso panga m'mbadwo uno.

Параўнаць

Даследуйце GENESIS 7:1

2

GENESIS 7:24

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo anapambana madzi padziko lapansi masiku zana kudza makumi asanu.

Параўнаць

Даследуйце GENESIS 7:24

3

GENESIS 7:11

Buku Lopatulika

BLP-2018

Chaka cha mazana asanu ndi limodzi cha moyo wa Nowa, mwezi wachiwiri, tsiku la khumi ndi asanu ndi awiri la mwezi, tsiku lomwelo akasupe onse a madzi aakulu anasefuka, ndi mazenera a kumwamba anatseguka.

Параўнаць

Даследуйце GENESIS 7:11

4

GENESIS 7:23

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo zinaonongedwa zamoyo zonse zimene zinali padziko lapansi, anthu, ndi nyama, ndi zokwawa, ndi mbalame za m'mlengalenga; ndipo zinaonongedwa padziko lapansi: anatsala Nowa yekha ndi amene anali pamodzi naye m'chingalawa.

Параўнаць

Даследуйце GENESIS 7:23

5

GENESIS 7:12

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo mvula inali padziko lapansi masiku makumi anai usana ndi usiku.

Параўнаць

Даследуйце GENESIS 7:12

Папярэдні разьдзел
Наступны разьдзел
YouVersion

Заахвочваем і заклікаем вас кожны дзень шукаць блізкасці з Богам.

Служэнне

Пра дадатак

Кар'ера

Валянтэрства

Блёг

Прэса

Карысныя спасылкі

Дапамога

Ахвяраваць

Пераклады

Аўдыё Бібліі

Мовы Бібліі

Верш дня


Лічбавае служэнне

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Палітыка прыватнасьціУмовы карыстаньня
Праграма раскрыцця ўразлівасцяў
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Стужка

Біблія

Планы чытання

Відэа