Luka 10:41-42

Luka 10:41-42 CCL

Ambuye anati, “Marita, Marita, ukudandaula ndi kuvutika ndi zinthu zambiri, koma chofunika nʼchimodzi chokha. Mariya wasankha chinthu chabwino, ndipo palibe angamulande chimenechi.”