Luka 14:34-35

Luka 14:34-35 CCL

“Mchere ndi wabwino, koma ngati usukuluka adzawukoleretsanso ndi chiyani? Suyeneranso ngakhale mʼnthaka kapena kudzala la manyowa; umatayidwa kunja. “Amene ali ndi makutu akumva, amve.”