YouVersion Logo
Search Icon

YOHANE 13:14-15

YOHANE 13:14-15 BLPB2014

Chifukwa chake, ngati Ine Ambuye ndi Mphunzitsi, ndasambitsa mapazi anu, inunso muyenera kusambitsana mapazi wina ndi mnzake. Pakuti ndakupatsani inu chitsanzo, kuti, monga Ine ndakuchitirani inu, inunso muchite.

Free Reading Plans and Devotionals related to YOHANE 13:14-15