YouVersion Logo
Search Icon

LUKA 16:11-12

LUKA 16:11-12 BLPB2014

Chifukwa chake ngati simunakhala okhulupirika m'chuma cha chosalungama, adzakhulupirira inu ndani ndi chuma choona? Ndipo ngati simunakhala okhulupirika ndi zake za wina, adzakupatsani inu ndani za inu eni?

Video for LUKA 16:11-12

Free Reading Plans and Devotionals related to LUKA 16:11-12