Logotip de YouVersion
La BíbliaPlansVídeos
Aconsegueix l'aplicació
Selector d'idiomes
Icona de cerca

Versets bíblics populars de YOHANE 9

1

YOHANE 9:4

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Tiyenera kugwira ntchito za Iye wondituma Ine, pokhala pali msana; ukudza usiku pamene palibe munthu angakhoze kugwira ntchito.

Compara

Explorar YOHANE 9:4

2

YOHANE 9:5

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Pakukhala Ine m'dziko lapansi, ndili kuunika kwa dziko lapansi.

Compara

Explorar YOHANE 9:5

3

YOHANE 9:2-3

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo ophunzira ake anamfunsa Iye, nanena, Rabi, anachimwa ndani, ameneyo, kapena atate wake ndi amake, kuti anabadwa wosaona? Yesu anayankha, Sanachimwe ameneyo, kapena atate wake ndi amake; koma kuti ntchito za Mulungu zikaonetsedwe mwa iye.

Compara

Explorar YOHANE 9:2-3

4

YOHANE 9:39

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yesu anati, Kudzaweruza ndadza Ine kudziko lino lapansi, kuti iwo osapenya apenye; ndi kuti iwo akupenya akhale osaona.

Compara

Explorar YOHANE 9:39

Plans de lectura i devocionals gratuïts relacionats amb YOHANE 9

Capítol anterior
Capítol següent
YouVersion

Animant-te i desafiant-te a buscar la intimitat amb Déu cada dia.

Ministeri

Sobre

Carreres

Fes-te voluntari

Blog

Premsa

Enllaços útils

Ajuda

Fer un donatiu

Versions de la Bíblia

Bíblia en àudio

Idiomes de la Bíblia

Verset del dia


Un Ministeri Digital de

Life.Church
Català

©2026 Life.Church / YouVersion

Política de privacitatCondicions d'ús
Programa de divulgació de vulnerabilitats
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest