YouVersion-logo
RaamattuSuunnitelmatVideot
Hanki sovellus
Kielen valitsin
Hakukuvake

Suosittuja jakeita Raamatun kirjasta GENESIS 7

1

GENESIS 7:1

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo anati Yehova kwa Nowa, Talowani, iwe ndi akunyumba ako onse m'chingalawamo; chifukwa ndakuona iwe kuti uli wolungama pamaso panga m'mbadwo uno.

Vertaa

Tutki GENESIS 7:1

2

GENESIS 7:24

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo anapambana madzi padziko lapansi masiku zana kudza makumi asanu.

Vertaa

Tutki GENESIS 7:24

3

GENESIS 7:11

Buku Lopatulika

BLP-2018

Chaka cha mazana asanu ndi limodzi cha moyo wa Nowa, mwezi wachiwiri, tsiku la khumi ndi asanu ndi awiri la mwezi, tsiku lomwelo akasupe onse a madzi aakulu anasefuka, ndi mazenera a kumwamba anatseguka.

Vertaa

Tutki GENESIS 7:11

4

GENESIS 7:23

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo zinaonongedwa zamoyo zonse zimene zinali padziko lapansi, anthu, ndi nyama, ndi zokwawa, ndi mbalame za m'mlengalenga; ndipo zinaonongedwa padziko lapansi: anatsala Nowa yekha ndi amene anali pamodzi naye m'chingalawa.

Vertaa

Tutki GENESIS 7:23

5

GENESIS 7:12

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo mvula inali padziko lapansi masiku makumi anai usana ndi usiku.

Vertaa

Tutki GENESIS 7:12

Edellinen luku
Seuraava luku
YouVersion

Rohkaisemassa ja haastamassa sinua etsimään läheisyyttä Jumalan kanssa joka päivä.

Palvelutehtävä

Tietoa

Uramahdollisuudet

Vapaaehtoiseksi

Blogi

Lehdistö

Hyödyllisiä linkkejä

Apua

Lahjoita

Raamatunkäännökset

Ääniraamatut

Kielet

Päivän jae


Digitaalinen palvelutehtävä

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

YksityisyyskäytännötKäyttöehdot
Haavoittuvuuden paljastamisohjelma
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Koti

Raamattu

Suunnitelmat

Videot