YouVersion-logo
RaamattuSuunnitelmatVideot
Hanki sovellus
Kielen valitsin
Hakukuvake

Suosittuja jakeita Raamatun kirjasta LUKA 10

1

LUKA 10:19

Buku Lopatulika

BLP-2018

Taonani, ndakupatsani ulamuliro wakuponda pa njoka ndi zinkhanira, ndi pa mphamvu iliyonse ya mdaniyo; ndipo kulibe kanthu kadzakuipsani konse.

Vertaa

Tutki LUKA 10:19

2

LUKA 10:41-42

Buku Lopatulika

BLP-2018

Koma Ambuye anayankha nati kwa iye, Marita, Marita, uda nkhawa nuvutika ndi zinthu zambiri; koma chisoweka chinthu chimodzi, pakuti Maria anasankha dera lokoma limene silidzachotsedwa kwa iye.

Vertaa

Tutki LUKA 10:41-42

3

LUKA 10:27

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo iye anayankha nati, Uzikonda Ambuye Mulungu wako ndi mtima wako wonse, ndi moyo wako wonse, ndi mphamvu yako yonse, ndi nzeru zako zonse, ndi mnansi wako monga iwe mwini.

Vertaa

Tutki LUKA 10:27

4

LUKA 10:2

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo ananena kwa iwo, Dzinthu dzichuluka, koma antchito achepa; potero pemphani Mwini dzinthu, kuti akankhe antchito kukututa kwake.

Vertaa

Tutki LUKA 10:2

5

LUKA 10:36-37

Buku Lopatulika

BLP-2018

Uti wa awa atatu, uyesa iwe, anakhala mnansi wa iye uja adagwa m'manja a achifwamba? Ndipo anati, Iye wakumchitira chifundo. Ndipo Yesu anati kwa iye, Pita nuchite iwe momwemo.

Vertaa

Tutki LUKA 10:36-37

6

LUKA 10:3

Buku Lopatulika

BLP-2018

Mukani; taonani, Ine ndituma inu ngati anaankhosa pakati pa mimbulu.

Vertaa

Tutki LUKA 10:3

Ilmaiset lukusuunnitelmat ja hartaudet liittyen aiheeseen LUKA 10

Edellinen luku
Seuraava luku
YouVersion

Rohkaisemassa ja haastamassa sinua etsimään läheisyyttä Jumalan kanssa joka päivä.

Palvelutehtävä

Tietoa

Uramahdollisuudet

Vapaaehtoiseksi

Blogi

Lehdistö

Hyödyllisiä linkkejä

Apua

Lahjoita

Raamatunkäännökset

Ääniraamatut

Kielet

Päivän jae


Digitaalinen palvelutehtävä

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

YksityisyyskäytännötKäyttöehdot
Haavoittuvuuden paljastamisohjelma
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Koti

Raamattu

Suunnitelmat

Videot