Logo de l'application Bible
Îcone de recherche

Matayo 5:29-30

Matayo 5:29-30 NTNYBL2025

Ngati diso lako la kwene likakuchiticha kuti uchite chimo lizule ni kulitaya kutali. Mbasa kutaiza chiwalo chimojhi cha thupi lako kusiyana ni thupi lako lonjhe kutaidwa ku jehanamu ya moto. Ngati jhanja lako la kwene likuchiticha kuti uchite chimo lidule ni ukalitaye kutali ni iwe. Mbasa kutaiza chiwalo chimojhi cha thupi lako kusiyana ni thupi lako lonjhe kutaidwa ku jehanamu ya moto.”

Vidéo pour Matayo 5:29-30

Plans de lecture et méditations gratuites relatifs àMatayo 5:29-30