לוגו של YouVersion
כתבי הקודשתכניותקטעי וידאו
הורד את האפליקציה
בורר שפה
סמל חיפוש

פסוקים פופולריים מ- LUKA 19

1

LUKA 19:10

Buku Lopatulika

BLP-2018

Pakuti Mwana wa Munthu anadza kufunafuna ndi kupulumutsa chotayikacho.

השווה

חקרו LUKA 19:10

2

LUKA 19:38

Buku Lopatulika

BLP-2018

nanena, Wolemekezeka Mfumuyo ikudza m'dzina la Ambuye; mtendere mu Mwamba, ndi ulemerero mu Mwambamwamba.

השווה

חקרו LUKA 19:38

3

LUKA 19:9

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Yesu anati kwa iye, Lero chipulumutso chagwera nyumba iyi, popeza iyenso ndiye mwana wa Abrahamu.

השווה

חקרו LUKA 19:9

4

LUKA 19:5-6

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo m'mene anadza pamalopo Yesu anakweza maso nati kwa iye, Zakeyo, fulumira, nutsike; pakuti lero ndiyenera kukhala m'nyumba mwako. Ndipo anafulumira, natsika, namlandira Iye wokondwera.

השווה

חקרו LUKA 19:5-6

5

LUKA 19:8

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Zakeyo anaimirira nati kwa Ambuye, Taonani, Ambuye, gawo limodzi la zanga zonse zogawika pakati ndipatsa osauka; ndipo ngati ndalanda kanthu kwa munthu monyenga, ndimbwezera kanai.

השווה

חקרו LUKA 19:8

6

LUKA 19:39-40

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Afarisi ena a m'khamu la anthu anati kwa Iye, Mphunzitsi, dzudzulani ophunzira anu. Ndipo anayankha nati, Ndinena ndi inu, ngati awa khala chete miyala idzafuula.

השווה

חקרו LUKA 19:39-40

תכניות קריאה חינמיות בנושא LUKA 19

לפרק הקודם
לפרק הבא
YouVersion

מעודד ומאתגר אתכם לקשר הדוק עם אלוהים בכל יום.

מִשׂרָד

אודות

קריירה

התנדב

בלוג

לחץ

קישורים שימושיים

עזרה

תרום

גרסאות הכתובים

אודיו הכתובים

שפות התנ"ך

הפסוק של היום


משרד דיגיטלי של

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

מדיניות פרטיותתנאים
תוכנית לגילוי חולשות אחראי
פייסבוקטוויטראינטגרםיוטיובפינטרסט

בית

כתבי הקודש

תכניות

קטעי וידאו