MACHITIDWE A ATUMWI 7:57-58

MACHITIDWE A ATUMWI 7:57-58 BLPB2014

Koma anafuula ndi mau akulu, natseka m'makutu mwao, namgumukira iye ndi mtima umodzi; ndipo anamtaya kunja kwa mudzi, namponya miyala; ndipo mbonizo zinaika zovala zao pa mapazi a mnyamata dzina lake Saulo.