YouVersion-ի լոգոն
ԱստվածաշունչԾրագրերՏեսանյութեր
Տեղադրեք հավելվածը
Ընտրել լեզուն
Որոնման պատկերակ

Աստվածաշնչի հայտնի հատվածներ GENESIS 4-ից

1

GENESIS 4:7

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ukachita zabwino, sudzalandiridwa kodi? Ukaleka kuchita zabwino, uchimo ubwatama pakhomo: kwa iwe kudzakhala kulakalaka kwake, ndipo iwe udzamlamulira iye.

Համեմատել

Ուսումնասիրեք GENESIS 4:7

2

GENESIS 4:26

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndiponso kwa Seti, kwa iye kunabadwa mwana wamwamuna: anamutcha dzina lake Enosi: pomwepo anthu anayamba kutchula dzina la Yehova.

Համեմատել

Ուսումնասիրեք GENESIS 4:26

3

GENESIS 4:9

Buku Lopatulika

BLP-2018

Yehova ndipo anati kwa Kaini, Ali kuti Abele mphwako? Ndipo anati, Sindidziwai: kodi ndine woyang'anira mphwanga?

Համեմատել

Ուսումնասիրեք GENESIS 4:9

4

GENESIS 4:10

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo anati, Wachita chiyani? Mau a mwazi wa mphwako andifuulira Ine kunthaka.

Համեմատել

Ուսումնասիրեք GENESIS 4:10

5

GENESIS 4:15

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Yehova anati kwa iye, Chifukwa chake aliyense amene adzapha Kaini kudzabwezedwa kwa iye kasanu ndi kawiri. Ndipo Yehova anaika chizindikiro pa Kaini, kuti asamuphe aliyense akampeza.

Համեմատել

Ուսումնասիրեք GENESIS 4:15

Նախորդ գլուխը
Հաջորդ գլուխը
YouVersion

Քաջալերում և մարտահրավեր ենք նետում Ձեզ Աստծո հետ մտերմանալու համար։

Ծառայություն

Մեր մասին

Աշխատատեղեր

Կամավոր

Բլոգ

Մամուլ

Օգտակար հղումներ

Օգնություն

Նվիրաբերել

Աստվածաշնչի տարբերակներ

Աուդիո Աստվածաշնչեր

Աստվածաշնչի լեզուներ

Օրվա խոսքը


Թվային ծառայություն

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Գաղտնիության քաղաքականությունՊայմանները
Խոցելիության բացահայտման ծրագիր
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Գլխավոր

Աստվածաշունչ

Ծրագրեր

Տեսանյութեր