Logo YouVersion
AlkitabRencanaVideo
Dapatkan Aplikasinya
Pemilih Bahasa
Ikon Pencarian

Ayat-ayat Alkitab Ternama dari GENESIS 2

1

GENESIS 2:24

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Chifukwa chotero mwamuna adzasiya atate wake ndi amake nadzadziphatika kwa mkazi wake: ndipo adzakhala thupi limodzi.

Bandingkan

Telusuri GENESIS 2:24

2

GENESIS 2:18

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Yehova Mulungu ndipo anati, Si kwabwino kuti munthu akhale yekha; ndidzampangira womthangatira iye.

Bandingkan

Telusuri GENESIS 2:18

3

GENESIS 2:7

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yehova Mulungu anaumba munthu ndi dothi lapansi, nauzira mpweya wa moyo m'mphuno mwake; munthuyo nakhala wamoyo.

Bandingkan

Telusuri GENESIS 2:7

4

GENESIS 2:23

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anati Adamu, Uyu tsopano ndiye fupa la mafupa anga, ndi mnofu wa mnofu wanga; ndipo adzatchedwa Mkazi, chifukwa anamtenga mwa mwamuna.

Bandingkan

Telusuri GENESIS 2:23

5

GENESIS 2:3

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mulungu ndipo anadalitsa tsiku lachisanu ndi chiwiri, naliyeretsa limenelo: chifukwa limenelo adapuma ku ntchito yake yonse imene Mulungu anailenga ndi kupanga.

Bandingkan

Telusuri GENESIS 2:3

6

GENESIS 2:25

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Onse awiri ndipo anali amaliseche, mwamuna ndi mkazi wake, ndipo analibe manyazi.

Bandingkan

Telusuri GENESIS 2:25

Rencana Bacaan dan Renungan gratis terkait dengan GENESIS 2

Pasal Sebelumnya
Pasal Berikutnya
YouVersion

Mendorong dan menantang Anda mencari keintiman dengan Tuhan setiap hari.

Pelayanan

Tentang

Karier

Sukarelawan

Blog

Pers

Tautan Berguna

Bantuan

Sumbang

Versi Alkitab

Alkitab Audio

Bahasa Alkitab

Ayat Hari Ini


Pelayanan Digital dari

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Kebijakan PrivasiSyarat
Program Pengungkapan Kerentanan
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Beranda

Alkitab

Rencana

Video