GENESIS 1:11

GENESIS 1:11 BLPB2014

Mulungu ndipo anati, Dziko lapansi limere udzu, therere lobala mbeu, ndi mtengo wazipatso wakubala zipatso monga mwa mtundu wake, momwemo muli mbeu yake, pa dziko lapansi: ndipo kunatero.

Rencana Bacaan dan Renungan gratis terkait dengan GENESIS 1:11