YouVersionロゴ
聖書読書プランビデオ
アプリを入手
言語選択
検索アイコン

YOHANE 2の有名な聖句

1

YOHANE 2:11

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Chiyambi ichi cha zizindikiro zake Yesu anachita m'Kana wa m'Galileya naonetsera ulemerero wake; ndipo ophunzira ake anakhulupirira Iye.

比較

YOHANE 2:11で検索

2

YOHANE 2:4

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Yesu nanena naye, Mkazi, ndili ndi chiyani ndi inu? Nthawi yanga siinafike.

比較

YOHANE 2:4で検索

3

YOHANE 2:7-8

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Yesu ananena nao, Dzazani mitsukoyo ndi madzi. Naidzaza, ndendende. Ndipo ananena nao, Tungani tsopano, mupite nao kwa mkulu wa phwando. Ndipo anapita nao.

比較

YOHANE 2:7-8で検索

4

YOHANE 2:19

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Yesu anayankha nati kwa iwo, Pasulani Kachisi uyu, ndipo masiku atatu ndidzamuutsa.

比較

YOHANE 2:19で検索

5

YOHANE 2:15-16

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo pamene adapanga mkwapulo wazingwe, anatulutsa onse m'Kachisimo, ndi nkhosa ndi ng'ombe; nakhuthula ndalama za osinthanawo, nagubuduza magome; nati kwa iwo akugulitsa nkhunda, Chotsani izi muno; musamayesa nyumba ya Atate wanga nyumba ya malonda.

比較

YOHANE 2:15-16で検索

無料の読書プランとYOHANE 2に関係したデボーション

前章
次章
YouVersion

日々、神との親しい交わりを求めるために、あなたを励まし、勇気を与えます。

ミニストリー

概要

キャリア

ボランティア

ブログ

プレス

便利なリンク集

ヘルプ

寄付

聖書の訳

オーディオ聖書

聖書の言語

今日の聖句


デジタルミニストリー

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

プライバシー規約利用規約
脆弱性の開示
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

ホーム

聖書

読書プラン

ビデオ