YouVersion 로고
성경묵상동영상
앱 다운로드
언어 선택
검색 아이콘

GENESIS 11 - 인기 성경 구절

1

GENESIS 11:6-7

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Yehova anati, Taonani, anthu ali amodzi, ndipo onse ali nacho chinenedwe chao chimodzi; ndipo ichi ayamba kuchita: ndipo tsopano palibe kanthu kakuletsedwa nao kamene akafuna kuchita. Tiyeni, titsike, pomwepo tisokoneze chinenedwe chao, kuti wina asamvere chinenedwe cha mnzake.

비교

GENESIS 11:6-7 살펴보기

2

GENESIS 11:4

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo anati, Tiyeni, timange mzinda ndi nsanja, pamutu pake pafikire kumwamba; ndipo tidzipangire ife tokha dzina kuti tisabalalike padziko lonse lapansi.

비교

GENESIS 11:4 살펴보기

3

GENESIS 11:9

Buku Lopatulika

BLP-2018

Chifukwa chake anatcha dzina lake Babiloni pakuti kumeneko Yehova anasokoneza chinenedwe cha dziko lonse lapansi; kuyambira pamenepo Yehova anabalalitsa iwo padziko lonse lapansi.

비교

GENESIS 11:9 살펴보기

4

GENESIS 11:1

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo dziko lapansi linali la chinenedwe chimodzi ndi chilankhulidwe chimodzi.

비교

GENESIS 11:1 살펴보기

5

GENESIS 11:5

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Yehova anatsikira kudzaona mzinda ndi nsanja imene analinkumanga ana a anthu.

비교

GENESIS 11:5 살펴보기

6

GENESIS 11:8

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Yehova anabalalitsa iwo padziko lonse lapansi, ndipo analeka kumanga mzinda.

비교

GENESIS 11:8 살펴보기

이전 장
다음 장
YouVersion

매일 하나님과 친밀하게 동행하도록 격려하고 도전하기.

사역

소개

채용 정보

자원 봉사

블로그

기사

유용한 링크

도움

후원

성경 번역본

오디오 성경

성경 언어

오늘의 말씀


디지털 사역

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

개인 정보 취급 정책약관
취약점 공개 프로그램
페이스북트위터인스타그램유튜브핀터레스트

홈

성경

묵상

동영상