YouVersion 로고
성경묵상동영상
앱 다운로드
언어 선택
검색 아이콘

YOHANE 7 - 인기 성경 구절

1

YOHANE 7:38

Buku Lopatulika

Iye wokhulupirira Ine, monga chilembo chinati, Mitsinje ya madzi amoyo idzayenda, kutuluka m'kati mwake.

비교

YOHANE 7:38 살펴보기

2

YOHANE 7:37

Buku Lopatulika

Koma tsiku lomaliza, lalikululo la chikondwerero, Yesu anaimirira nafuula, ndi kunena, Ngati pali munthu akumva ludzu, adze kwa Ine, namwe.

비교

YOHANE 7:37 살펴보기

3

YOHANE 7:39

Buku Lopatulika

Koma ichi anati za Mzimu, amene iwo akukhulupirira Iye anati adzalandire; pakuti Mzimu panalibe pamenepo, chifukwa Yesu sanalemekezedwe panthawi pomwepo.

비교

YOHANE 7:39 살펴보기

4

YOHANE 7:24

Buku Lopatulika

Musaweruze monga maonekedwe, koma weruzani chiweruziro cholungama.

비교

YOHANE 7:24 살펴보기

5

YOHANE 7:18

Buku Lopatulika

Iye wolankhula zochokera kwa iye yekha afuna ulemu wa mwini yekha. Iye wakufuna ulemu wa Iye amene anamtuma, yemweyu ali woona, ndipo mwa Iye mulibe chosalungama.

비교

YOHANE 7:18 살펴보기

6

YOHANE 7:16

Buku Lopatulika

Pamenepo Yesu anayankha iwo, nati, Chiphunzitso changa sichili changa, koma cha Iye amene anandituma Ine.

비교

YOHANE 7:16 살펴보기

7

YOHANE 7:7

Buku Lopatulika

Dziko lapansi silingathe kudana ndi inu; koma Ine lindida popeza Ine ndilichitira umboni, kuti ntchito zake zili zoipa.

비교

YOHANE 7:7 살펴보기

YOHANE 7: 관련 무료 묵상 계획

이전 장
다음 장
YouVersion

매일 하나님과 친밀하게 동행하도록 격려하고 도전하기.

사역

소개

채용 정보

자원 봉사

블로그

기사

유용한 링크

도움

후원

성경 번역본

오디오 성경

성경 언어

오늘의 말씀


디지털 사역

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

개인 정보 취급 정책약관
취약점 공개 프로그램
페이스북트위터인스타그램유튜브핀터레스트

홈

성경

묵상

동영상