YouVersion 로고
성경묵상동영상
앱 다운로드
언어 선택
검색 아이콘

LUKA 16 - 인기 성경 구절

1

LUKA 16:10

Buku Lopatulika

BLP-2018

Iye amene akhulupirika m'chaching'onong'ono alinso wokhulupirika m'chachikulu; ndipo iye amene ali wosalungama m'chachikulu.

비교

LUKA 16:10 살펴보기

2

LUKA 16:13

Buku Lopatulika

BLP-2018

Palibe mnyamata wa m'nyumba akhoza kukhala kapolo wa ambuye awiri; pakuti kapena adzamuda wina, nadzakonda winayo; kapena adzatsata wina, nadzapeputsa winayo. Simungathe kukhala kapolo wa Mulungu ndi wa Chuma.

비교

LUKA 16:13 살펴보기

3

LUKA 16:11-12

Buku Lopatulika

BLP-2018

Chifukwa chake ngati simunakhale okhulupirika m'chuma cha chosalungama, adzakhulupirira inu ndani ndi chuma choona? Ndipo ngati simunakhale okhulupirika ndi zake za wina, adzakupatsani inu ndani za inu eni?

비교

LUKA 16:11-12 살펴보기

4

LUKA 16:31

Buku Lopatulika

BLP-2018

Koma anati kwa iye, Ngati samvera Mose ndi aneneri, sadzakopeka mtima ngakhale wina akauka kwa akufa.

비교

LUKA 16:31 살펴보기

5

LUKA 16:18

Buku Lopatulika

BLP-2018

Yense wakusudzula mkazi wake, nakwatira wina, achita chigololo; ndipo iye amene akwatira wosudzulidwayo, achita chigololo.

비교

LUKA 16:18 살펴보기

LUKA 16: 관련 무료 묵상 계획

이전 장
다음 장
YouVersion

매일 하나님과 친밀하게 동행하도록 격려하고 도전하기.

사역

소개

채용 정보

자원 봉사

블로그

기사

유용한 링크

도움

후원

성경 번역본

오디오 성경

성경 언어

오늘의 말씀


디지털 사역

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

개인 정보 취급 정책약관
취약점 공개 프로그램
페이스북트위터인스타그램유튜브핀터레스트

홈

성경

묵상

동영상