YouVersion 로고
성경묵상동영상
앱 다운로드
언어 선택
검색 아이콘

LUKA 19 - 인기 성경 구절

1

LUKA 19:10

Buku Lopatulika

BLP-2018

Pakuti Mwana wa Munthu anadza kufunafuna ndi kupulumutsa chotayikacho.

비교

LUKA 19:10 살펴보기

2

LUKA 19:38

Buku Lopatulika

BLP-2018

nanena, Wolemekezeka Mfumuyo ikudza m'dzina la Ambuye; mtendere mu Mwamba, ndi ulemerero mu Mwambamwamba.

비교

LUKA 19:38 살펴보기

3

LUKA 19:9

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Yesu anati kwa iye, Lero chipulumutso chagwera nyumba iyi, popeza iyenso ndiye mwana wa Abrahamu.

비교

LUKA 19:9 살펴보기

4

LUKA 19:5-6

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo m'mene anadza pamalopo Yesu anakweza maso nati kwa iye, Zakeyo, fulumira, nutsike; pakuti lero ndiyenera kukhala m'nyumba mwako. Ndipo anafulumira, natsika, namlandira Iye wokondwera.

비교

LUKA 19:5-6 살펴보기

5

LUKA 19:8

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Zakeyo anaimirira nati kwa Ambuye, Taonani, Ambuye, gawo limodzi la zanga zonse zogawika pakati ndipatsa osauka; ndipo ngati ndalanda kanthu kwa munthu monyenga, ndimbwezera kanai.

비교

LUKA 19:8 살펴보기

6

LUKA 19:39-40

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Afarisi ena a m'khamu la anthu anati kwa Iye, Mphunzitsi, dzudzulani ophunzira anu. Ndipo anayankha nati, Ndinena ndi inu, ngati awa khala chete miyala idzafuula.

비교

LUKA 19:39-40 살펴보기

LUKA 19: 관련 무료 묵상 계획

이전 장
다음 장
YouVersion

매일 하나님과 친밀하게 동행하도록 격려하고 도전하기.

사역

소개

채용 정보

자원 봉사

블로그

기사

유용한 링크

도움

후원

성경 번역본

오디오 성경

성경 언어

오늘의 말씀


디지털 사역

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

개인 정보 취급 정책약관
취약점 공개 프로그램
페이스북트위터인스타그램유튜브핀터레스트

홈

성경

묵상

동영상