YouVersion 로고
성경묵상동영상
앱 다운로드
언어 선택
검색 아이콘

YOHANE 5 - 인기 성경 구절

1

YOHANE 5:24

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Indetu, indetu, ndinena kwa inu, kuti iye wakumva mau anga, ndi kukhulupirira Iye amene anandituma Ine, ali nao moyo wosatha, ndipo salowa m'kuweruza, koma wachokera kuimfa, nalowa m'moyo.

비교

YOHANE 5:24 살펴보기

2

YOHANE 5:6

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Yesu, pakuona ameneyo alikugona, ndipo anadziwa kuti anatero nthawi yaikulu pamenepo, ananena naye, Ufuna kuchiritsidwa kodi?

비교

YOHANE 5:6 살펴보기

3

YOHANE 5:39-40

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Musanthula m'malembo, popeza muyesa kuti momwemo muli nao moyo wosatha; ndipo akundichitira Ine umboni ndi iwo omwewo; ndipo simufuna kudza kwa Ine, kuti mukhale nao moyo.

비교

YOHANE 5:39-40 살펴보기

4

YOHANE 5:8-9

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Yesu ananena naye, Tauka, yalula mphasa yako, nuyende. Ndipo pomwepo munthuyu anachira, nayalula mphasa yake, nayenda. Koma tsiku lomwelo linali la Sabata.

비교

YOHANE 5:8-9 살펴보기

5

YOHANE 5:19

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamenepo Yesu anayankha nati kwa iwo, Indetu, indetu ndinena kwa inu, sakhoza Mwana kuchita kanthu pa yekha, koma chimene aona Atate achichita, ndicho. Pakuti zimene Iye azichita, zomwezo Mwananso azichita momwemo.

비교

YOHANE 5:19 살펴보기

YOHANE 5: 관련 무료 묵상 계획

이전 장
다음 장
YouVersion

매일 하나님과 친밀하게 동행하도록 격려하고 도전하기.

사역

소개

채용 정보

자원 봉사

블로그

기사

유용한 링크

도움

후원

성경 번역본

오디오 성경

성경 언어

오늘의 말씀


디지털 사역

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

개인 정보 취급 정책약관
취약점 공개 프로그램
페이스북트위터인스타그램유튜브핀터레스트

홈

성경

묵상

동영상