YouVersion logo
BijbelLeesplannenVideo's
Download de app
Taalkiezer
Zoek icoon

Populaire Bijbelverzen uit YOHANE 13

1

YOHANE 13:34-35

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndikupatsani inu lamulo latsopano, kuti mukondane wina ndi mnzake; monga ndakonda inu, kuti inunso mukondane wina ndi mnzake. Mwa ichi adzazindikira onse kuti muli ophunzira anga, ngati muli nacho chikondano wina ndi mnzake.

Vergelijk

Ontdek YOHANE 13:34-35

2

YOHANE 13:14-15

Buku Lopatulika

BLP-2018

Chifukwa chake, ngati Ine Ambuye ndi Mphunzitsi, ndasambitsa mapazi anu, inunso muyenera kusambitsana mapazi wina ndi mnzake. Pakuti ndakupatsani inu chitsanzo, kuti, monga Ine ndakuchitirani inu, inunso muchite.

Vergelijk

Ontdek YOHANE 13:14-15

3

YOHANE 13:7

Buku Lopatulika

BLP-2018

Yesu anayankha nati kwa iye, Chimene ndichita Ine suchidziwa tsopano; koma udzadziwa m'tsogolo mwake.

Vergelijk

Ontdek YOHANE 13:7

4

YOHANE 13:16

Buku Lopatulika

BLP-2018

Indetu, indetu, ndinena ndi inu, Kapolo sali wamkulu ndi mbuye wake; kapena mtumwi sali wamkulu ndi womtuma iye.

Vergelijk

Ontdek YOHANE 13:16

5

YOHANE 13:17

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ngati mudziwa izi, odala inu ngati muzichita.

Vergelijk

Ontdek YOHANE 13:17

6

YOHANE 13:4-5

Buku Lopatulika

BLP-2018

ananyamuka pamgonero, navula malaya ake; ndipo m'mene adatenga chopukutira, anadzimanga m'chuuno. Pomwepo anathira madzi m'beseni, nayamba kusambitsa mapazi a ophunzira ake, ndi kuwapukuta ndi chopukutira, chimene anadzimanga nacho.

Vergelijk

Ontdek YOHANE 13:4-5

Gratis leesplannen en overdenkingen die te maken hebben met YOHANE 13

Vorig hoofdstuk
Volgend hoofdstuk
YouVersion

Moedigt jou aan en daagt je uit om elke dag gemeenschap met God te zoeken.

Bediening

Over

Carrières

Vrijwilliger

Blog

Pers

Nuttige links

Help

Bijdragen

Bijbelvertalingen

Luisterbijbels

Bijbeltalen

Tekst van de Dag


Een digitale bediening van

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

PrivacybeleidVoorwaarden
Programma voor openbaarmaking van kwetsbaarheden
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Thuisscherm

Bijbel

Leesplannen

Video's