YouVersion logo
BijbelLeesplannenVideo's
Download de app
Taalkiezer
Zoek icoon

Populaire Bijbelverzen uit LUKA 24

1

LUKA 24:49

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo onani, Ine nditumiza pa inu lonjezano la Atate wanga; koma khalani inu m'mzinda muno, kufikira mwavekedwa ndi mphamvu yochokera Kumwamba.

Vergelijk

Ontdek LUKA 24:49

2

LUKA 24:6

Buku Lopatulika

BLP-2018

Palibe kuno Iye, komatu anauka; kumbukirani muja adalankhula nanu, pamene analinso mu Galileya

Vergelijk

Ontdek LUKA 24:6

3

LUKA 24:31-32

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo maso ao anatseguka, ndipo anamzindikira Iye; ndipo anawakanganukira Iye, nawachokera. Ndipo anati wina kwa mnzake, Mtima wathu sunali wotentha m'kati mwathu nanga m'mene analankhula nafe m'njira, m'mene anatitsegulira malembo?

Vergelijk

Ontdek LUKA 24:31-32

4

LUKA 24:46-47

Buku Lopatulika

BLP-2018

ndipo anati kwa iwo, Kotero kwalembedwa, kuti Khristu amve zowawa, nauke kwa akufa tsiku lachitatu; ndi kuti kulalikidwe m'dzina lake kulapa ndi kukhululukidwa kwa machimo kwa mitundu yonse, kuyambira ku Yerusalemu.

Vergelijk

Ontdek LUKA 24:46-47

5

LUKA 24:2-3

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo anapeza mwala unakunkhunizidwa kuuchotsa pamanda. Ndipo m'mene analowa sanapeze mtembo wa Ambuye Yesu.

Vergelijk

Ontdek LUKA 24:2-3

Vorig hoofdstuk
Volgend hoofdstuk
YouVersion

Moedigt jou aan en daagt je uit om elke dag gemeenschap met God te zoeken.

Bediening

Over

Carrières

Vrijwilliger

Blog

Pers

Nuttige links

Help

Bijdragen

Bijbelvertalingen

Luisterbijbels

Bijbeltalen

Tekst van de Dag


Een digitale bediening van

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

PrivacybeleidVoorwaarden
Programma voor openbaarmaking van kwetsbaarheden
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Thuisscherm

Bijbel

Leesplannen

Video's