Logo YouVersion
BibliaPlanyNagrania wideo
Pobierz aplikację
Wybór języka
Ikona wyszukiwania

Popularne wersety biblijne z GENESIS 7

1

GENESIS 7:1

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo anati Yehova kwa Nowa, Talowani, iwe ndi akunyumba ako onse m'chingalawamo; chifukwa ndakuona iwe kuti uli wolungama pamaso panga m'mbadwo uno.

Porównaj

Przeglądaj GENESIS 7:1

2

GENESIS 7:24

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo anapambana madzi padziko lapansi masiku zana kudza makumi asanu.

Porównaj

Przeglądaj GENESIS 7:24

3

GENESIS 7:11

Buku Lopatulika

BLP-2018

Chaka cha mazana asanu ndi limodzi cha moyo wa Nowa, mwezi wachiwiri, tsiku la khumi ndi asanu ndi awiri la mwezi, tsiku lomwelo akasupe onse a madzi aakulu anasefuka, ndi mazenera a kumwamba anatseguka.

Porównaj

Przeglądaj GENESIS 7:11

4

GENESIS 7:23

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo zinaonongedwa zamoyo zonse zimene zinali padziko lapansi, anthu, ndi nyama, ndi zokwawa, ndi mbalame za m'mlengalenga; ndipo zinaonongedwa padziko lapansi: anatsala Nowa yekha ndi amene anali pamodzi naye m'chingalawa.

Porównaj

Przeglądaj GENESIS 7:23

5

GENESIS 7:12

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo mvula inali padziko lapansi masiku makumi anai usana ndi usiku.

Porównaj

Przeglądaj GENESIS 7:12

Poprzedni rozdział
Następny rozdział
YouVersion

Zachęcanie i wzywanie cię do codziennego szukania bliskości z Bogiem.

Misja

O YouVersion

Praca

Wolontariat

Blog

Prasa

Przydatne linki

Pomoc

Wesprzyj

Przekłady Biblii

Biblie audio

Języki Biblii

Werset dnia


Cyfrowa misja

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Polityka prywatnościRegulamin
Program ujawniania luk w zabezpieczeniach
FacebookTwitterInstagramYoutubePinterest

Strona główna

Biblia

Plany

Nagrania wideo