YouVersion logga
BibelnLäsplanerVideor
Skaffa appen
Språkväljare
Sök ikon

Populära bibelverser från GENESIS 2

1

GENESIS 2:24

Buku Lopatulika

BLP-2018

Chifukwa chotero mwamuna adzasiya atate wake ndi amake nadzadziphatika kwa mkazi wake: ndipo adzakhala thupi limodzi.

Jämför

Utforska GENESIS 2:24

2

GENESIS 2:18

Buku Lopatulika

BLP-2018

Yehova Mulungu ndipo anati, Si kwabwino kuti munthu akhale yekha; ndidzampangira womthangatira iye.

Jämför

Utforska GENESIS 2:18

3

GENESIS 2:7

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Yehova Mulungu anaumba munthu ndi dothi lapansi, nauzira mpweya wa moyo m'mphuno mwake; munthuyo nakhala wamoyo.

Jämför

Utforska GENESIS 2:7

4

GENESIS 2:23

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo anati Adamu, Uyu tsopano ndiye fupa la mafupa anga, ndi mnofu wa mnofu wanga; ndipo adzatchedwa Mkazi, chifukwa anamtenga mwa mwamuna.

Jämför

Utforska GENESIS 2:23

5

GENESIS 2:3

Buku Lopatulika

BLP-2018

Mulungu ndipo anadalitsa tsiku lachisanu ndi chiwiri, naliyeretsa limenelo: chifukwa limenelo adapuma ku ntchito yake yonse imene Mulungu anailenga ndi kupanga.

Jämför

Utforska GENESIS 2:3

6

GENESIS 2:25

Buku Lopatulika

BLP-2018

Onse awiri ndipo anali amaliseche, mwamuna ndi mkazi wake, ndipo analibe manyazi.

Jämför

Utforska GENESIS 2:25

Gratis läsplaner och andakter relaterade till GENESIS 2

Föregående kapitel
Nästa kapitel
YouVersion

Uppmuntrar och utmanar dig att söka Guds närhet varje dag.

Tjänst

Om

Karriärer

Volontär

Blogg

Press

Användbara länkar

Hjälp

Donera

Bibelöversättningar

Ljudbiblar

Bibelspråk

Dagens vers


En digital tjänst från

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

IntegritetspolicyVillkor
Åtgärdsprogram för säkerhet
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Hem

Bibeln

Läsplaner

Videor