YouVersion Logosu
Kutsal KitapOkuma PlanlarıVideolar
Uygulamayı Yükle
Dil Seçicisi
Arama Simgesi

YOHANE 17 Popüler Kutsal Kitap Ayetleri

1

YOHANE 17:17

Buku Lopatulika

Patulani iwo m'choonadi; mau anu ndi choonadi.

Karşılaştır

YOHANE 17:17 keşfedin

2

YOHANE 17:3

Buku Lopatulika

Koma moyo wosatha ndi uwu, kuti akadziwe Inu Mulungu woona yekha, ndi Yesu Khristu amene munamtuma.

Karşılaştır

YOHANE 17:3 keşfedin

3

YOHANE 17:20-21

Buku Lopatulika

Koma sindipempherera iwo okha, komanso iwo akukhulupirira Ine chifukwa cha mau ao; kuti onse akakhale amodzi, monga Inu Atate mwa Ine, ndi Ine mwa Inu, kuti iwonso akakhale mwa Ife: kuti dziko lapansi likakhulupirire kuti Inu munandituma Ine.

Karşılaştır

YOHANE 17:20-21 keşfedin

4

YOHANE 17:15

Buku Lopatulika

Sindipempha kuti muwachotse iwo m'dziko lapansi, koma kuti muwasunge iwo kuletsa woipayo.

Karşılaştır

YOHANE 17:15 keşfedin

5

YOHANE 17:22-23

Buku Lopatulika

Ndipo ulemerero umene mwandipatsa Ine ndapatsa iwo; kuti akhale amodzi, monga Ife tili mmodzi; Ine mwa iwo, ndi Inu mwa Ine, kuti akhale angwiro mwa mmodzi; kuti dziko lapansi lizindikire kuti Inu munandituma Ine, nimunawakonda iwo, monga momwe munakonda Ine.

Karşılaştır

YOHANE 17:22-23 keşfedin

YOHANE 17 ile ilgili ücretsiz Okuma Planları ve Teşvik Yazıları

Önceki Bölüm
Sonraki Bölüm
YouVersion

Her gün Tanrı ile daha derin bir ilişki için sizi cesaretlendiriyor ve bu mücadeleye davet ediyoruz.

Hizmet

Hakkında

Kariyer

Gönüllü Ol

Blog

Basın

Yararlı Bağlantılar

Yardım

Bağışta bulun

Kutsal Kitap Çevirileri

Sesli Kutsal Kitaplar

Kutsal Kitap Dilleri

Günün Ayeti


Dijital Bir Hizmeti

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Gizlilik PolitikasıKoşullar
Güvenlik Açığı Bildirim Programı
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Ana Sayfa

Kutsal Kitap

Okuma Planları

Videolar