YouVersion Logosu
Kutsal KitapOkuma PlanlarıVideolar
Uygulamayı Yükle
Dil Seçicisi
Arama Simgesi

GENESIS 18 Popüler Kutsal Kitap Ayetleri

1

GENESIS 18:14

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Kodi chilipo chinthu chomkanika Yehova? Pa nthawi yoikidwa ndidzabwera kwa iwe, pakufika nyengo yake, ndipo Sara adzakhala ndi mwana wamwamuna.

Karşılaştır

GENESIS 18:14 keşfedin

2

GENESIS 18:12

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

ndipo Sara anaseka m'mtima mwake, nati, Kodi ndidzakhala ndi kukondwa ine nditakalamba, ndiponso mbuyanga ali wokalamba?

Karşılaştır

GENESIS 18:12 keşfedin

3

GENESIS 18:18

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Pakuti Abrahamu adzakhala ndithu wamkulu ndi wamphamvu, ndipo mitundu yonse ya dziko lapansi idzadalitsika mwa iye?

Karşılaştır

GENESIS 18:18 keşfedin

4

GENESIS 18:23-24

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Abrahamu anayandikira nati, Kodi mudzaononga olungama pamodzi ndi oipa? Kapena alipo olungama makumi asanu m'kati mwa mudzi; kodi mudzaononga, simudzasiya malowo chifukwa cha olungama makumi asanu ali momwemo?

Karşılaştır

GENESIS 18:23-24 keşfedin

5

GENESIS 18:26

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anati Yehova, Ndikapeza m'Sodomu olungama makumi asanu m'kati mwa mudzi, ndidzasiya malo onse chifukwa cha iwo.

Karşılaştır

GENESIS 18:26 keşfedin

Önceki Bölüm
Sonraki Bölüm
YouVersion

Her gün Tanrı ile daha derin bir ilişki için sizi cesaretlendiriyor ve bu mücadeleye davet ediyoruz.

Hizmet

Hakkında

Kariyer

Gönüllü Ol

Blog

Basın

Yararlı Bağlantılar

Yardım

Bağışta bulun

Kutsal Kitap Çevirileri

Sesli Kutsal Kitaplar

Kutsal Kitap Dilleri

Günün Ayeti


Dijital Bir Hizmeti

Life.Church
Türkçe

©2026 Life.Church / YouVersion

Gizlilik PolitikasıKoşullar
Güvenlik Açığı Bildirim Programı
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest