YouVersion Logosu
Kutsal KitapOkuma PlanlarıVideolar
Uygulamayı Yükle
Dil Seçicisi
Arama Simgesi

GENESIS 2 Popüler Kutsal Kitap Ayetleri

1

GENESIS 2:24

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Chifukwa chotero mwamuna adzasiya atate wake ndi amake nadzadziphatika kwa mkazi wake: ndipo adzakhala thupi limodzi.

Karşılaştır

GENESIS 2:24 keşfedin

2

GENESIS 2:18

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Yehova Mulungu ndipo anati, Si kwabwino kuti munthu akhale yekha; ndidzampangira womthangatira iye.

Karşılaştır

GENESIS 2:18 keşfedin

3

GENESIS 2:7

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yehova Mulungu anaumba munthu ndi dothi lapansi, nauzira mpweya wa moyo m'mphuno mwake; munthuyo nakhala wamoyo.

Karşılaştır

GENESIS 2:7 keşfedin

4

GENESIS 2:23

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anati Adamu, Uyu tsopano ndiye fupa la mafupa anga, ndi mnofu wa mnofu wanga; ndipo adzatchedwa Mkazi, chifukwa anamtenga mwa mwamuna.

Karşılaştır

GENESIS 2:23 keşfedin

5

GENESIS 2:3

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Mulungu ndipo anadalitsa tsiku lachisanu ndi chiwiri, naliyeretsa limenelo: chifukwa limenelo adapuma ku ntchito yake yonse imene Mulungu anailenga ndi kupanga.

Karşılaştır

GENESIS 2:3 keşfedin

6

GENESIS 2:25

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Onse awiri ndipo anali amaliseche, mwamuna ndi mkazi wake, ndipo analibe manyazi.

Karşılaştır

GENESIS 2:25 keşfedin

GENESIS 2 ile ilgili ücretsiz Okuma Planları ve Teşvik Yazıları

Önceki Bölüm
Sonraki Bölüm
YouVersion

Her gün Tanrı ile daha derin bir ilişki için sizi cesaretlendiriyor ve bu mücadeleye davet ediyoruz.

Hizmet

Hakkında

Kariyer

Gönüllü Ol

Blog

Basın

Yararlı Bağlantılar

Yardım

Bağışta bulun

Kutsal Kitap Çevirileri

Sesli Kutsal Kitaplar

Kutsal Kitap Dilleri

Günün Ayeti


Dijital Bir Hizmeti

Life.Church
Türkçe

©2026 Life.Church / YouVersion

Gizlilik PolitikasıKoşullar
Güvenlik Açığı Bildirim Programı
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest