Biểu trưng YouVersion
Biểu tượng Tìm kiếm

YOHANE 21:6

YOHANE 21:6 BLP-2018

Koma anati kwa iwo, Ponyani khoka kumbali ya dzanja lamanja ya ngalawa, ndipo mudzapeza. Pamenepo anaponya, ndipo analibenso mphamvu yakulikoka chifukwa cha kuchuluka nsomba.