1
Gen. 16:13
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
Tsono Hagara adatcha Chauta amene adalankhula naye kuti, “Inu ndinu Mulungu wondipenya,” poti adati, “Pano ndamuwona Iye amene amandipenya.”
對照
探尋 Gen. 16:13
2
Gen. 16:11
Popitiriza mau mngeloyo adati, “Tsopano uli pafupi kukhala ndi mwana wamwamuna, udzamutche Ismaele, ndiye kuti Chauta wamva kulira kwako pa zovuta zako.
探尋 Gen. 16:11
3
Gen. 16:12
Koma mwana wako adzakhala ndi mtima wa chilombo, adzadana ndi aliyense, ndipo anthu onse adzadana naye. Adzakhala akudana ndi abale ake onse.”
探尋 Gen. 16:12
首頁
聖經
計畫
視訊