1
GENESIS 10:8
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Ndipo Kusi anabala Nimirodi; ndipo iye anayamba kukhala wamphamvu pa dziko lapansi.
አወዳድር
{{ጥቅስ}} ያስሱ
2
GENESIS 10:9
Iye ndiye mpalu wamphamvu pamaso pa Yehova: chifukwa chake kunanenedwa, Monga Nimirodi mpalu wamphamvu pamaso pa Yehova.
ቤት
መጽሐፍ ቅዱስ
እቅዶች
ቪዲዮዎች