1
EKSODO 1:17
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Koma anamwino anaopa Mulungu, ndipo sanachite monga mfumu ya Aejipito inawauza, koma analeka ana amuna akhale ndi moyo.
مقایسه
EKSODO 1:17 را جستجو کنید
2
EKSODO 1:12
Koma monga momwe anawasautsiramo, momwemo anachuluka, momwemonso anafalikira. Ndipo anavutika chifukwa cha ana Israele.
EKSODO 1:12 را جستجو کنید
3
EKSODO 1:21
Ndipo kunatero kuti, popeza anamwino anaopa Mulungu, Iye anawamangitsira mabanja.
EKSODO 1:21 را جستجو کنید
4
EKSODO 1:8
Pamenepo inalowa mfumu yatsopano m'ufumu wa Ejipito, imene siinadziwa Yosefe.
EKSODO 1:8 را جستجو کنید