لوگو یوورژن
كتاب‌ مقدسبرنامه‌های مطالعهویدیوها
دانلود برنامه
انتخاب زبان
ایکن جستجو

آیات محبوب کتاب مقدس از GENESIS 4

1

GENESIS 4:7

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ukachita zabwino, sudzalandiridwa kodi? Ukaleka kuchita zabwino, uchimo ubwatama pakhomo: kwa iwe kudzakhala kulakalaka kwake, ndipo iwe udzamlamulira iye.

مقایسه

GENESIS 4:7 را جستجو کنید

2

GENESIS 4:26

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndiponso kwa Seti, kwa iye kunabadwa mwana wamwamuna: anamutcha dzina lake Enosi: pomwepo anthu anayamba kutchula dzina la Yehova.

مقایسه

GENESIS 4:26 را جستجو کنید

3

GENESIS 4:9

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Yehova ndipo anati kwa Kaini, Ali kuti Abele mphwako? Ndipo anati, Sindidziwai: kodi ndine woyang'anira mphwanga?

مقایسه

GENESIS 4:9 را جستجو کنید

4

GENESIS 4:10

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anati, Wachita chiyani? Mau a mwazi wa mphwako andifuulira Ine kunthaka.

مقایسه

GENESIS 4:10 را جستجو کنید

5

GENESIS 4:15

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yehova anati kwa iye, Chifukwa chake aliyense amene adzapha Kaini kudzabwezedwa kwa iye kasanu ndi kawiri. Ndipo Yehova anaika chizindikiro pa Kaini, kuti asamuphe aliyense akampeza.

مقایسه

GENESIS 4:15 را جستجو کنید

باب‌ قبلی
باب بعدی
یوورژن

به چالش کشیدن و تشویق هر روزه شما برای ایجاد رابطه صمیمی تر با خدا .

خدمت

دربارهٔ

مشاغل

داوطلب شوید.

بلاگ

مطبوعات

لینک‌های مفید

پشتیبانی

اهدای کمک مالی

ترجمه‌های کتاب‌مقدس

کتاب‌ مقدس صوتی

ترجمه‌های موجود کتاب‌مقس

آیۀ روز


یک خدمت دیجیتالی از

لایف‌چرچ
English (US)

©2025 لایف چرچ / یوورژن

قوانین حفظ حریم شخصیشرايط
برنامه افشای آسیب پذیری
فیس‌بوکتویتراینستاگرامبرنامه یوتیوببرنامه پین ترست

خانه

كتاب‌ مقدس

برنامه‌های مطالعه

ویدیوها