לוגו של YouVersion
כתבי הקודשתכניותקטעי וידאו
הורד את האפליקציה
בורר שפה
סמל חיפוש

פסוקים פופולריים מ- YOHANE 7

1

YOHANE 7:38

Buku Lopatulika

BLP-2018

Iye wokhulupirira Ine, monga chilembo chinati, Mitsinje ya madzi amoyo idzayenda, kutuluka m'kati mwake.

השווה

חקרו YOHANE 7:38

2

YOHANE 7:37

Buku Lopatulika

BLP-2018

Koma tsiku lomaliza, lalikululo la chikondwerero, Yesu anaimirira nafuula, ndi kunena, Ngati pali munthu akumva ludzu, adze kwa Ine, namwe.

השווה

חקרו YOHANE 7:37

3

YOHANE 7:39

Buku Lopatulika

BLP-2018

Koma ichi anati za Mzimu, amene iwo akukhulupirira Iye anati adzalandire; pakuti Mzimu panalibe pamenepo, chifukwa Yesu sanalemekezedwe panthawi pomwepo.

השווה

חקרו YOHANE 7:39

4

YOHANE 7:24

Buku Lopatulika

BLP-2018

Musaweruze monga maonekedwe, koma weruzani chiweruziro cholungama.

השווה

חקרו YOHANE 7:24

5

YOHANE 7:18

Buku Lopatulika

BLP-2018

Iye wolankhula zochokera kwa iye yekha afuna ulemu wa mwini yekha. Iye wakufuna ulemu wa Iye amene anamtuma, yemweyu ali woona, ndipo mwa Iye mulibe chosalungama.

השווה

חקרו YOHANE 7:18

6

YOHANE 7:16

Buku Lopatulika

BLP-2018

Pamenepo Yesu anayankha iwo, nati, Chiphunzitso changa sichili changa, koma cha Iye amene anandituma Ine.

השווה

חקרו YOHANE 7:16

7

YOHANE 7:7

Buku Lopatulika

BLP-2018

Dziko lapansi silingathe kudana ndi inu; koma Ine lindida popeza Ine ndilichitira umboni, kuti ntchito zake zili zoipa.

השווה

חקרו YOHANE 7:7

תכניות קריאה חינמיות בנושא YOHANE 7

לפרק הקודם
לפרק הבא
YouVersion

מעודד ומאתגר אתכם לקשר הדוק עם אלוהים בכל יום.

מִשׂרָד

אודות

קריירה

התנדב

בלוג

לחץ

קישורים שימושיים

עזרה

תרום

גרסאות הכתובים

אודיו הכתובים

שפות התנ"ך

הפסוק של היום


משרד דיגיטלי של

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

מדיניות פרטיותתנאים
תוכנית לגילוי חולשות אחראי
פייסבוקטוויטראינטגרםיוטיובפינטרסט

בית

כתבי הקודש

תכניות

קטעי וידאו