לוגו של YouVersion
כתבי הקודשתכניותקטעי וידאו
הורד את האפליקציה
בורר שפה
סמל חיפוש

פסוקים פופולריים מ- YOHANE 8

1

YOHANE 8:12

Buku Lopatulika

BLP-2018

Pamenepo Yesu analankhulanso nao, nanena, Ine ndine kuunika kwa dziko lapansi; iye wonditsata Ine sadzayenda mumdima, koma adzakhala nako kuunika kwa moyo.

השווה

חקרו YOHANE 8:12

2

YOHANE 8:32

Buku Lopatulika

BLP-2018

ndipo mudzazindikira choonadi, ndipo choonadi chidzakumasulani.

השווה

חקרו YOHANE 8:32

3

YOHANE 8:31

Buku Lopatulika

BLP-2018

Chifukwa chake Yesu ananena kwa Ayuda aja adakhulupirira Iye, Ngati mukhala inu m'mau anga, muli ophunzira anga ndithu

השווה

חקרו YOHANE 8:31

4

YOHANE 8:36

Buku Lopatulika

BLP-2018

Chifukwa chake ngati Mwana adzakuyesani inu aufulu, mudzakhala mfulu ndithu.

השווה

חקרו YOHANE 8:36

5

YOHANE 8:7

Buku Lopatulika

BLP-2018

Koma pamene anakhalakhala alikumfunsabe Iye, anaweramuka, nati kwa iwo, Amene mwa inu ali wopanda tchimo, ayambe kumponya mwala.

השווה

חקרו YOHANE 8:7

6

YOHANE 8:34

Buku Lopatulika

BLP-2018

Yesu anayankha iwo, nati, Indetu, indetu, ndinena kwa inu kuti yense wakuchita tchimo ali kapolo wa tchimolo.

השווה

חקרו YOHANE 8:34

7

YOHANE 8:10-11

Buku Lopatulika

BLP-2018

Koma Yesu pamene adaweramuka, anati kwa iye, Mkazi iwe, ali kuti ajawa? Palibe munthu anakutsutsa kodi? Koma iye anati, Palibe, Ambuye. Ndipo Yesu anati, Inenso sindikutsutsa iwe; pita; kuyambira tsopano usachimwenso.

השווה

חקרו YOHANE 8:10-11

לפרק הקודם
לפרק הבא
YouVersion

מעודד ומאתגר אתכם לקשר הדוק עם אלוהים בכל יום.

מִשׂרָד

אודות

קריירה

התנדב

בלוג

לחץ

קישורים שימושיים

עזרה

תרום

גרסאות הכתובים

אודיו הכתובים

שפות התנ"ך

הפסוק של היום


משרד דיגיטלי של

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

מדיניות פרטיותתנאים
תוכנית לגילוי חולשות אחראי
פייסבוקטוויטראינטגרםיוטיובפינטרסט

בית

כתבי הקודש

תכניות

קטעי וידאו