YouVersion-ի լոգոն
ԱստվածաշունչԾրագրերՏեսանյութեր
Տեղադրեք հավելվածը
Ընտրել լեզուն
Որոնման պատկերակ

Աստվածաշնչի հայտնի հատվածներ GENESIS 7-ից

1

GENESIS 7:1

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo anati Yehova kwa Nowa, Talowani, iwe ndi akunyumba ako onse m'chingalawamo; chifukwa ndakuona iwe kuti uli wolungama pamaso panga m'mbadwo uno.

Համեմատել

Ուսումնասիրեք GENESIS 7:1

2

GENESIS 7:24

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo anapambana madzi padziko lapansi masiku zana kudza makumi asanu.

Համեմատել

Ուսումնասիրեք GENESIS 7:24

3

GENESIS 7:11

Buku Lopatulika

BLP-2018

Chaka cha mazana asanu ndi limodzi cha moyo wa Nowa, mwezi wachiwiri, tsiku la khumi ndi asanu ndi awiri la mwezi, tsiku lomwelo akasupe onse a madzi aakulu anasefuka, ndi mazenera a kumwamba anatseguka.

Համեմատել

Ուսումնասիրեք GENESIS 7:11

4

GENESIS 7:23

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo zinaonongedwa zamoyo zonse zimene zinali padziko lapansi, anthu, ndi nyama, ndi zokwawa, ndi mbalame za m'mlengalenga; ndipo zinaonongedwa padziko lapansi: anatsala Nowa yekha ndi amene anali pamodzi naye m'chingalawa.

Համեմատել

Ուսումնասիրեք GENESIS 7:23

5

GENESIS 7:12

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo mvula inali padziko lapansi masiku makumi anai usana ndi usiku.

Համեմատել

Ուսումնասիրեք GENESIS 7:12

Նախորդ գլուխը
Հաջորդ գլուխը
YouVersion

Քաջալերում և մարտահրավեր ենք նետում Ձեզ Աստծո հետ մտերմանալու համար։

Ծառայություն

Մեր մասին

Աշխատատեղեր

Կամավոր

Բլոգ

Մամուլ

Օգտակար հղումներ

Օգնություն

Նվիրաբերել

Աստվածաշնչի տարբերակներ

Աուդիո Աստվածաշնչեր

Աստվածաշնչի լեզուներ

Օրվա խոսքը


Թվային ծառայություն

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Գաղտնիության քաղաքականությունՊայմանները
Խոցելիության բացահայտման ծրագիր
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Գլխավոր

Աստվածաշունչ

Ծրագրեր

Տեսանյութեր