YouVersion-ի լոգոն
ԱստվածաշունչԾրագրերՏեսանյութեր
Տեղադրեք հավելվածը
Ընտրել լեզուն
Որոնման պատկերակ

Աստվածաշնչի հայտնի հատվածներ GENESIS 8-ից

1

GENESIS 8:21-22

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Yehova anamva chonunkhira chakukondweretsa; nati Yehova m'mtima mwake, Sindidzatembereranso konse nthaka chifukwa cha munthu; pakuti ndingaliro ya mtima wa munthu ili yoipa kuyambira pa unyamata wake; sindidzaphanso konse zinthu zonse zamoyo, monga momwe ndachitiramo. Pakukhalabe masiku a dziko lapansi, nthawi yakubzala ndi yakukunkha, chisanu ndi mafundi, malimwe ndi msakasa, usana ndi usiku sizidzalekai.

Համեմատել

Ուսումնասիրեք GENESIS 8:21-22

2

GENESIS 8:20

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Nowa anamanga guwa la nsembe la Yehova; natengapo nyama zodyedwa zonse ndi mbalame zodyedwa zonse napereka nsembe zopsereza paguwapo.

Համեմատել

Ուսումնասիրեք GENESIS 8:20

3

GENESIS 8:1

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Mulungu anakumbukira Nowa ndi zamoyo zonse, ndi nyama zonse zimene zinali pamodzi naye m'chingalawamo; ndipo Mulungu anapititsa mphepo padziko lapansi, naphwa madzi

Համեմատել

Ուսումնասիրեք GENESIS 8:1

4

GENESIS 8:11

Buku Lopatulika

BLP-2018

ndipo njiwa inadza kwa iye madzulo; ndipo, taonani, m'kamwa mwake munali tsamba la azitona lothyoledwa: ndipo anadziwa Nowa kuti madzi analimkuphwa padziko lapansi.

Համեմատել

Ուսումնասիրեք GENESIS 8:11

Նախորդ գլուխը
Հաջորդ գլուխը
YouVersion

Քաջալերում և մարտահրավեր ենք նետում Ձեզ Աստծո հետ մտերմանալու համար։

Ծառայություն

Մեր մասին

Աշխատատեղեր

Կամավոր

Բլոգ

Մամուլ

Օգտակար հղումներ

Օգնություն

Նվիրաբերել

Աստվածաշնչի տարբերակներ

Աուդիո Աստվածաշնչեր

Աստվածաշնչի լեզուներ

Օրվա խոսքը


Թվային ծառայություն

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Գաղտնիության քաղաքականությունՊայմանները
Խոցելիության բացահայտման ծրագիր
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Գլխավոր

Աստվածաշունչ

Ծրագրեր

Տեսանյութեր