1
GENESIS 7:1
Buku Lopatulika
Ndipo anati Yehova kwa Nowa, Talowani, iwe ndi akunyumba ako onse m'chingalawamo; chifukwa ndakuona iwe kuti uli wolungama pamaso panga m'mbadwo uno.
താരതമ്യം
GENESIS 7:1 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
2
GENESIS 7:24
Ndipo anapambana madzi padziko lapansi masiku zana kudza makumi asanu.
GENESIS 7:24 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
3
GENESIS 7:11
Chaka cha mazana asanu ndi limodzi cha moyo wa Nowa, mwezi wachiwiri, tsiku la khumi ndi asanu ndi awiri la mwezi, tsiku lomwelo akasupe onse a madzi aakulu anasefuka, ndi mazenera a kumwamba anatseguka.
GENESIS 7:11 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
4
GENESIS 7:23
Ndipo zinaonongedwa zamoyo zonse zimene zinali padziko lapansi, anthu, ndi nyama, ndi zokwawa, ndi mbalame za m'mlengalenga; ndipo zinaonongedwa padziko lapansi: anatsala Nowa yekha ndi amene anali pamodzi naye m'chingalawa.
GENESIS 7:23 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
5
GENESIS 7:12
Ndipo mvula inali padziko lapansi masiku makumi anai usana ndi usiku.
GENESIS 7:12 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
ഭവനം
വേദപുസ്തകം
പദ്ധതികൾ
വീഡിയോകൾ