Logo YouVersion
AlkitabPelanVideo
Dapatkan apl
Pemilih Bahasa
Ikon Carian

Ayat Alkitab yang Popular daripada GENESIS 11

1

GENESIS 11:6-7

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yehova anati, Taonani, anthu ali amodzi, ndipo onse ali nacho chinenedwe chao chimodzi; ndipo ichi ayamba kuchita: ndipo tsopano palibe kanthu kakuletsedwa nao kamene akafuna kuchita. Tiyeni, titsike, pomwepo tisokoneze chinenedwe chao, kuti wina asamvere chinenedwe cha mnzake.

Bandingkan

Selidiki GENESIS 11:6-7

2

GENESIS 11:4

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anati, Tiyeni, timange mudzi ndi nsanja, pamutu pake pafikire kumwamba; ndipo tidzipangire ife tokha dzina kuti tisabalalike pa dziko lonse lapansi.

Bandingkan

Selidiki GENESIS 11:4

3

GENESIS 11:9

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Chifukwa chake anatcha dzina lake Babele; pakuti kumeneko Yehova anasokoneza chinenedwe cha dziko lonse lapansi; kuyambira pamenepo Yehova anabalalitsa iwo pa dziko lonse lapansi.

Bandingkan

Selidiki GENESIS 11:9

4

GENESIS 11:1

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo dziko lapansi linali la chinenedwe chimodzi ndi chilankhulidwe chimodzi.

Bandingkan

Selidiki GENESIS 11:1

5

GENESIS 11:5

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yehova anatsikira kudzaona mudzi ndi nsanja imene analinkumanga ana a anthu.

Bandingkan

Selidiki GENESIS 11:5

6

GENESIS 11:8

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yehova anabalalitsa iwo pa dziko lonse lapansi, ndipo analeka kumanga mudzi.

Bandingkan

Selidiki GENESIS 11:8

Bab Sebelumnya
Bab Seterusnya
YouVersion

Mendorong dan mencabar anda untuk mencari hubungan rapat dengan Allah setiap hari.

Pelayanan

Perihal

Kerjaya

Jadi Sukarelawan

Blog

Akhbar

Pautan Berguna

Bantuan

Menderma

Versi Alkitab

Alkitab Audio

Bahasa Alkitab

Ayat Hari Ini


Pelayanan Digital

Life.Church
Bahasa Melayu

©2026 Life.Church / YouVersion

Polisi PrivasiTerma
Program Pendedahan Kerentanan
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest