Logo YouVersion
AlkitabPelanVideo
Dapatkan apl
Pemilih Bahasa
Ikon Carian

Ayat Alkitab yang Popular daripada GENESIS 7

1

GENESIS 7:1

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anati Yehova kwa Nowa, Talowani, iwe ndi akunyumba ako onse m'chingalawamo; chifukwa ndakuona iwe kuti uli wolungama pamaso panga m'mbadwo uno.

Bandingkan

Selidiki GENESIS 7:1

2

GENESIS 7:24

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anapambana madzi pa dziko lapansi masiku zana kudza makumi asanu.

Bandingkan

Selidiki GENESIS 7:24

3

GENESIS 7:11

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Chaka cha mazana asanu ndi limodzi cha moyo wa Nowa, mwezi wachiwiri, tsiku la khumi ndi asanu ndi awiri la mwezi, tsiku lomwelo akasupe onse a madzi aakulu anasefuka, ndi mazenera a kumwamba anatseguka.

Bandingkan

Selidiki GENESIS 7:11

4

GENESIS 7:23

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo zinaonongedwa zamoyo zonse zimene zinali pa dziko lapansi, anthu, ndi nyama, ndi zokwawa, ndi mbalame za m'mlengalenga; ndipo zinaonongedwa pa dziko lapansi: anatsala Nowa yekha ndi amene anali pamodzi naye m'chingalawa.

Bandingkan

Selidiki GENESIS 7:23

5

GENESIS 7:12

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo mvula inali pa dziko lapansi masiku makumi anai usana ndi usiku.

Bandingkan

Selidiki GENESIS 7:12

Bab Sebelumnya
Bab Seterusnya
YouVersion

Mendorong dan mencabar anda untuk mencari hubungan rapat dengan Allah setiap hari.

Pelayanan

Perihal

Kerjaya

Jadi Sukarelawan

Blog

Akhbar

Pautan Berguna

Bantuan

Menderma

Versi Alkitab

Alkitab Audio

Bahasa Alkitab

Ayat Hari Ini


Pelayanan Digital

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Polisi PrivasiTerma
Program Pendedahan Kerentanan
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Halaman Utama

Alkitab

Pelan

Video