YouVersion logo
BijbelLeesplannenVideo's
Download de app
Taalkiezer
Zoek icoon

Populaire Bijbelverzen uit YOHANE 8

1

YOHANE 8:12

Buku Lopatulika

BLP-2018

Pamenepo Yesu analankhulanso nao, nanena, Ine ndine kuunika kwa dziko lapansi; iye wonditsata Ine sadzayenda mumdima, koma adzakhala nako kuunika kwa moyo.

Vergelijk

Ontdek YOHANE 8:12

2

YOHANE 8:32

Buku Lopatulika

BLP-2018

ndipo mudzazindikira choonadi, ndipo choonadi chidzakumasulani.

Vergelijk

Ontdek YOHANE 8:32

3

YOHANE 8:31

Buku Lopatulika

BLP-2018

Chifukwa chake Yesu ananena kwa Ayuda aja adakhulupirira Iye, Ngati mukhala inu m'mau anga, muli ophunzira anga ndithu

Vergelijk

Ontdek YOHANE 8:31

4

YOHANE 8:36

Buku Lopatulika

BLP-2018

Chifukwa chake ngati Mwana adzakuyesani inu aufulu, mudzakhala mfulu ndithu.

Vergelijk

Ontdek YOHANE 8:36

5

YOHANE 8:7

Buku Lopatulika

BLP-2018

Koma pamene anakhalakhala alikumfunsabe Iye, anaweramuka, nati kwa iwo, Amene mwa inu ali wopanda tchimo, ayambe kumponya mwala.

Vergelijk

Ontdek YOHANE 8:7

6

YOHANE 8:34

Buku Lopatulika

BLP-2018

Yesu anayankha iwo, nati, Indetu, indetu, ndinena kwa inu kuti yense wakuchita tchimo ali kapolo wa tchimolo.

Vergelijk

Ontdek YOHANE 8:34

7

YOHANE 8:10-11

Buku Lopatulika

BLP-2018

Koma Yesu pamene adaweramuka, anati kwa iye, Mkazi iwe, ali kuti ajawa? Palibe munthu anakutsutsa kodi? Koma iye anati, Palibe, Ambuye. Ndipo Yesu anati, Inenso sindikutsutsa iwe; pita; kuyambira tsopano usachimwenso.

Vergelijk

Ontdek YOHANE 8:10-11

Gratis leesplannen en overdenkingen die te maken hebben met YOHANE 8

Vorig hoofdstuk
Volgend hoofdstuk
YouVersion

Moedigt jou aan en daagt je uit om elke dag gemeenschap met God te zoeken.

Bediening

Over

Carrières

Vrijwilliger

Blog

Pers

Nuttige links

Help

Bijdragen

Bijbelvertalingen

Luisterbijbels

Bijbeltalen

Tekst van de Dag


Een digitale bediening van

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

PrivacybeleidVoorwaarden
Programma voor openbaarmaking van kwetsbaarheden
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Thuisscherm

Bijbel

Leesplannen

Video's