YouVersion logo
BijbelLeesplannenVideo's
Download de app
Taalkiezer
Zoek icoon

Populaire Bijbelverzen uit YOHANE 9

1

YOHANE 9:4

Buku Lopatulika

BLP-2018

Tiyenera kugwira ntchito za Iye wondituma Ine, pokhala pali msana; ukudza usiku pamene palibe munthu angakhoze kugwira ntchito.

Vergelijk

Ontdek YOHANE 9:4

2

YOHANE 9:5

Buku Lopatulika

BLP-2018

Pakukhala Ine m'dziko lapansi, ndili kuunika kwa dziko lapansi.

Vergelijk

Ontdek YOHANE 9:5

3

YOHANE 9:2-3

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo ophunzira ake anamfunsa Iye, nanena, Rabi, anachimwa ndani, ameneyo, kapena atate wake ndi amake, kuti anabadwa wosaona? Yesu anayankha, Sanachimwe ameneyo, kapena atate wake ndi amake; koma kuti ntchito za Mulungu zikaonetsedwe mwa iye.

Vergelijk

Ontdek YOHANE 9:2-3

4

YOHANE 9:39

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Yesu anati, Kudzaweruza ndadza Ine kudziko lino lapansi, kuti iwo osapenya apenye; ndi kuti iwo akupenya akhale osaona.

Vergelijk

Ontdek YOHANE 9:39

Gratis leesplannen en overdenkingen die te maken hebben met YOHANE 9

Vorig hoofdstuk
Volgend hoofdstuk
YouVersion

Moedigt jou aan en daagt je uit om elke dag gemeenschap met God te zoeken.

Bediening

Over

Carrières

Vrijwilliger

Blog

Pers

Nuttige links

Help

Bijdragen

Bijbelvertalingen

Luisterbijbels

Bijbeltalen

Tekst van de Dag


Een digitale bediening van

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

PrivacybeleidVoorwaarden
Programma voor openbaarmaking van kwetsbaarheden
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Thuisscherm

Bijbel

Leesplannen

Video's