YouVersion logo
BijbelLeesplannenVideo's
Download de app
Taalkiezer
Zoek icoon

Populaire Bijbelverzen uit GENESIS 4

1

GENESIS 4:7

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ukachita zabwino, sudzalandiridwa kodi? Ukaleka kuchita zabwino, uchimo ubwatama pakhomo: kwa iwe kudzakhala kulakalaka kwake, ndipo iwe udzamlamulira iye.

Vergelijk

Ontdek GENESIS 4:7

2

GENESIS 4:26

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndiponso kwa Seti, kwa iye kunabadwa mwana wamwamuna: anamutcha dzina lake Enosi: pomwepo anthu anayamba kutchula dzina la Yehova.

Vergelijk

Ontdek GENESIS 4:26

3

GENESIS 4:9

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Yehova ndipo anati kwa Kaini, Ali kuti Abele mphwako? Ndipo anati, Sindidziwai: kodi ndine woyang'anira mphwanga?

Vergelijk

Ontdek GENESIS 4:9

4

GENESIS 4:10

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anati, Wachita chiyani? Mau a mwazi wa mphwako andifuulira Ine kunthaka.

Vergelijk

Ontdek GENESIS 4:10

5

GENESIS 4:15

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yehova anati kwa iye, Chifukwa chake aliyense amene adzapha Kaini kudzabwezedwa kwa iye kasanu ndi kawiri. Ndipo Yehova anaika chizindikiro pa Kaini, kuti asamuphe aliyense akampeza.

Vergelijk

Ontdek GENESIS 4:15

Gratis leesplannen en overdenkingen die te maken hebben met GENESIS 4

Vorig hoofdstuk
Volgend hoofdstuk
YouVersion

Moedigt jou aan en daagt je uit om elke dag gemeenschap met God te zoeken.

Bediening

Over

Carrières

Vrijwilliger

Blog

Pers

Nuttige links

Help

Bijdragen

Bijbelvertalingen

Luisterbijbels

Bijbeltalen

Tekst van de Dag


Een digitale bediening van

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

PrivacybeleidVoorwaarden
Programma voor openbaarmaking van kwetsbaarheden
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Thuisscherm

Bijbel

Leesplannen

Video's