Logótipo YouVersion
Ícone de pesquisa

YOHANE 21:18

YOHANE 21:18 BLPB2014

Indetu, indetu, ndinena ndi iwe, pamene unali mnyamata unadzimangira wekha m'chuuno, ndipo unayenda kumene unafuna; koma pamene udzakalamba udzatulutsa manja ako, ndipo adzakumanga wina, nadzakunyamula kumene sufuna.