YouVersion logga
BibelnLäsplanerVideor
Skaffa appen
Språkväljare
Sök ikon

Populära bibelverser från LUKA 24

1

LUKA 24:49

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo onani, Ine nditumiza pa inu lonjezano la Atate wanga; koma khalani inu m'mudzi muno, kufikira mwavekedwa ndi mphamvu yochokera Kumwamba.

Jämför

Utforska LUKA 24:49

2

LUKA 24:6

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Palibe kuno Iye, komatu anauka; kumbukirani muja adalankhula nanu, pamene analinso m'Galileya

Jämför

Utforska LUKA 24:6

3

LUKA 24:31-32

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo maso ao anatseguka, ndipo anamzindikira Iye; ndipo anawakanganukira Iye, nawachokera. Ndipo anati wina kwa mnzake, Mtima wathu sunali wotentha m'kati mwathu nanga m'mene analankhula nafe m'njira, m'mene anatitsegulira malembo?

Jämför

Utforska LUKA 24:31-32

4

LUKA 24:46-47

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

ndipo anati kwa iwo, Kotero kwalembedwa, kuti Khristu amve zowawa, nauke kwa akufa tsiku lachitatu; ndi kuti kulalikidwe m'dzina lake kulapa ndi kukhululukidwa kwa machimo kwa mitundu yonse, kuyambira ku Yerusalemu.

Jämför

Utforska LUKA 24:46-47

5

LUKA 24:2-3

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anapeza mwala unakunkhunizidwa kuuchotsa pamanda. Ndipo m'mene analowa sanapeze mtembo wa Ambuye Yesu.

Jämför

Utforska LUKA 24:2-3

Föregående kapitel
Nästa kapitel
YouVersion

Uppmuntrar och utmanar dig att söka Guds närhet varje dag.

Tjänst

Om

Karriärer

Volontär

Blogg

Press

Användbara länkar

Hjälp

Donera

Bibelöversättningar

Ljudbiblar

Bibelspråk

Dagens vers


En digital tjänst från

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

IntegritetspolicyVillkor
Åtgärdsprogram för säkerhet
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Hem

Bibeln

Läsplaner

Videor