1
Lk. 13:24
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
“Yesetsani kuloŵera pa khomo lophaphatiza, pakuti kunena zoona anthu ambiri adzafuna kuloŵa, koma adzalephera.
Jämför
Utforska Lk. 13:24
2
Lk. 13:11-12
M'menemo munali mai wina amene anali ndi mzimu woipa umene udamudwalitsa zaka 18. Anali ndi msana wokhota, mwakuti sankatha konse kuŵeramuka. Pamene Yesu adamuwona, adamuitana namuuza kuti, “Mai inu, mwamasuka ku matenda anu.”
Utforska Lk. 13:11-12
3
Lk. 13:13
Adamsanjika manja, ndipo pompo maiyo adaongoka, nayamba kutamanda Mulungu.
Utforska Lk. 13:13
4
Lk. 13:30
Pamenepo amene ali otsirizira adzakhala oyambirira, ndipo amene ali oyambirira adzakhala otsirizira.”
Utforska Lk. 13:30
5
Lk. 13:25
“Mwini nyumba adzanyamuka nkutseka pa khomo. Pamenepo, okhala panjanu mudzayamba kugogoda nkumanena kuti, ‘Ambuye, titsekulireni.’ Koma Iye adzakuyankhani kuti, ‘Sindikudziŵa kumene mukuchokera.’
Utforska Lk. 13:25
6
Lk. 13:5
Iyai, koma mukapanda kutembenuka mtima, inunso mudzaonongedwa ngati iwo aja.”
Utforska Lk. 13:5
7
Lk. 13:27
Koma Iye adzakuuzani kuti, ‘Pepani, sindikudziŵa kumene mukuchokera. Chokani apa nonsenu, anthu ochita zoipa.’
Utforska Lk. 13:27
8
Lk. 13:18-19
Yesu adati, “Kodi Ufumu wa Mulungu uli ngati chiyani, ndipo ndingauyerekeze ndi chiyani? Uli ngati njere ya mbeu ya mpiru imene munthu adakaifesa m'munda mwake. Idamera nisanduka mtengo, mbalame zamumlengalenga nkumabwera kudzamanga zisa pa nthambi zake.”
Utforska Lk. 13:18-19
Hem
Bibeln
Planer
Videor