YouVersion 标志
圣经计划视频
获取软件
选择语言
搜索图标

Matayo 2 的热门经文

1

Matayo 2:11

Nyanja

NTNYBL2025

Ndiipo adalowa mnyumba ni adamuona mwana pamojhi ni Maliya maye wake. Adagwada ni kumlambila. Adamasula mbhaso zao ni kumpacha mwana zaabu ni ubani ni mnghwala uwo utanidwa manemane.

对照

探索 Matayo 2:11

2

Matayo 2:1-2

Nyanja

NTNYBL2025

Yesu wadabadwa ku mujhi wa Beselehemu mjhiko la Yudea. Ndhawi imeneyo Helode wadali mfumu. Yesu yapo wadandobadwa wandhu yawo amajhiwa icho sichichokele adafika ku Yelusalemu adaafunjha, “Walikuti mwana uyo wabadwa Mfumu wa Ayahudi? Pakuti tayiona ndhondwa yake kudela la kumwela ni nafenjho tajha kumulambila.”

对照

探索 Matayo 2:1-2

3

Matayo 2:10

Nyanja

NTNYBL2025

Yapo adaiona ndhondwa ijha adakondwa kupunda.

对照

探索 Matayo 2:10

4

Matayo 2:12-13

Nyanja

NTNYBL2025

Ndiipo Mnungu adaonya kumaloto kuti asadabwelela kwa Helode. Chimwecho adabwela kujhiko lawo kwa kupitila njila yina. Wandhu yapo adatochoka mtumiki wa Ambuye wadamujhela Yusufu kumaloto ni kumkambila kuti, “Nyamuka umutenge mwana ni maye wake mthawile Kumisili. Mkakhale kumweko mbaka yapo sinikukambile pakuti Helode wafuna kuti wamphe mwanayo.”

对照

探索 Matayo 2:12-13

上一章
下一章
YouVersion

我们要鼓励、挑战你每天亲近上帝。

事工

关于我们

就职机会

义工

博客

新闻区

有用链接

帮助

捐赠

圣经译本

音频圣经

译本语言

今日经文


此数字事工属于

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

隐私政策使用条款
漏洞披露方案
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

主页

圣经

计划

视频