I-Logo ye-YouVersion
IBhayibheliAmapulaniAmavidiyo
Thola i App
Okukhetha Ulimi
Isici soku Sesha

Amavesi eBhayibheli adumile avela kokuthi YOHANE 7

1

YOHANE 7:38

Buku Lopatulika

BLP-2018

Iye wokhulupirira Ine, monga chilembo chinati, Mitsinje ya madzi amoyo idzayenda, kutuluka m'kati mwake.

Qhathanisa

Hlola YOHANE 7:38

2

YOHANE 7:37

Buku Lopatulika

BLP-2018

Koma tsiku lomaliza, lalikululo la chikondwerero, Yesu anaimirira nafuula, ndi kunena, Ngati pali munthu akumva ludzu, adze kwa Ine, namwe.

Qhathanisa

Hlola YOHANE 7:37

3

YOHANE 7:39

Buku Lopatulika

BLP-2018

Koma ichi anati za Mzimu, amene iwo akukhulupirira Iye anati adzalandire; pakuti Mzimu panalibe pamenepo, chifukwa Yesu sanalemekezedwe panthawi pomwepo.

Qhathanisa

Hlola YOHANE 7:39

4

YOHANE 7:24

Buku Lopatulika

BLP-2018

Musaweruze monga maonekedwe, koma weruzani chiweruziro cholungama.

Qhathanisa

Hlola YOHANE 7:24

5

YOHANE 7:18

Buku Lopatulika

BLP-2018

Iye wolankhula zochokera kwa iye yekha afuna ulemu wa mwini yekha. Iye wakufuna ulemu wa Iye amene anamtuma, yemweyu ali woona, ndipo mwa Iye mulibe chosalungama.

Qhathanisa

Hlola YOHANE 7:18

6

YOHANE 7:16

Buku Lopatulika

BLP-2018

Pamenepo Yesu anayankha iwo, nati, Chiphunzitso changa sichili changa, koma cha Iye amene anandituma Ine.

Qhathanisa

Hlola YOHANE 7:16

7

YOHANE 7:7

Buku Lopatulika

BLP-2018

Dziko lapansi silingathe kudana ndi inu; koma Ine lindida popeza Ine ndilichitira umboni, kuti ntchito zake zili zoipa.

Qhathanisa

Hlola YOHANE 7:7

Isahluko esedlule
Isahluko esilandelayo
I-YouVersion'

Ukukukhuthaza nokukubekela inselelo yokufuna ubudlelwano noNkulunkulu nsuku zonke.

Inkonzo

Mayelana

Imisebenzi

Volontiya

I-Blogi

Abezindaba

Izixhumanisi Eziwusizo

Usizo

Nikela

Izinguqulo zeBhayibheli

AmaBhayibheli Alalelwayo

Izilwimi zeBhayibheli

Ivesi losuku


Inkonzo yedijithali ye

Life.Church
English (US)

©2025 I-Life.Church / YouVersion

Inqubomgomo yobumfihloImibandela
Uhlelo Lokudalula Ubungozi
U-FacebookU-TwitterI-InstagramI-YouTubeI-Pinterest

Ikhaya

IBhayibheli

Amapulani

Amavidiyo