I-Logo ye-YouVersion
IBhayibheliAmapulaniAmavidiyo
Thola i App
Okukhetha Ulimi
Isici soku Sesha

Amavesi eBhayibheli adumile avela kokuthi LUKA 23

1

LUKA 23:34

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Yesu ananena, Atate, muwakhululukire iwo, pakuti sadziwa chimene achita. Ndipo anagawana zovala zake, poyesa maere.

Qhathanisa

Hlola LUKA 23:34

2

LUKA 23:43

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Iye ananena naye, Indetu, ndinena ndi iwe, Lero lino udzakhala ndine mu Paradaiso.

Qhathanisa

Hlola LUKA 23:43

3

LUKA 23:42

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo ananena, Yesu, ndikumbukireni m'mene mulowa Ufumu wanu.

Qhathanisa

Hlola LUKA 23:42

4

LUKA 23:46

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo pamene Yesu anafuula ndi mau aakulu, anati, Atate, m'manja mwanu ndipereka mzimu wanga. Ndipo pakutero anapereka mzimu wake.

Qhathanisa

Hlola LUKA 23:46

5

LUKA 23:33

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo pamene anafika kumalo dzina lake Bade, anampachika Iye pamtanda pomwepo, ndi ochita zoipa omwe, mmodzi kudzanja lamanja ndi wina kulamanzere.

Qhathanisa

Hlola LUKA 23:33

6

LUKA 23:44-45

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo ora lake pamenepo linali ngati lachisanu ndi chimodzi. Ndipo panali mdima padziko lonse kufikira ora lachisanu ndi chinai, ndipo dzuwa linada. Ndipo nsalu yotchinga ya mu Kachisi inang'ambika pakati.

Qhathanisa

Hlola LUKA 23:44-45

7

LUKA 23:47

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo pamene kenturiyo anaona chinachitikacho, analemekeza Mulungu, nanena, Zoonadi munthu uyu anali wolungama.

Qhathanisa

Hlola LUKA 23:47

Isahluko esedlule
Isahluko esilandelayo
I-YouVersion'

Ukukukhuthaza nokukubekela inselelo yokufuna ubudlelwano noNkulunkulu nsuku zonke.

Inkonzo

Mayelana

Imisebenzi

Volontiya

I-Blogi

Abezindaba

Izixhumanisi Eziwusizo

Usizo

Nikela

Izinguqulo zeBhayibheli

AmaBhayibheli Alalelwayo

Izilwimi zeBhayibheli

Ivesi losuku


Inkonzo yedijithali ye

Life.Church
English (US)

©2025 I-Life.Church / YouVersion

Inqubomgomo yobumfihloImibandela
Uhlelo Lokudalula Ubungozi
U-FacebookU-TwitterI-InstagramI-YouTubeI-Pinterest

Ikhaya

IBhayibheli

Amapulani

Amavidiyo