1
AROMA 13:14
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Koma valani inu Ambuye Yesu Khristu, ndipo musaganizire za thupi kuchita zofuna zake.
Compare
Explore AROMA 13:14
2
AROMA 13:8
Musakhale ndi mangawa kwa munthu aliyense, koma kukondana ndiko; pakuti iye amene akondana ndi mnzake wakwanitsa lamulo.
Explore AROMA 13:8
3
AROMA 13:1
Anthu onse amvere maulamuliro a akulu; pakuti palibe ulamuliro wina koma wochokera kwa Mulungu; ndipo iwo amene alipo aikidwa ndi Mulungu.
Explore AROMA 13:1
4
AROMA 13:12
Usiku wapita, ndi mbandakucha wayandikira; chifukwa chake tivule ntchito za mdima, ndipo tivale zida za kuunika.
Explore AROMA 13:12
5
AROMA 13:10
Chikondano sichichitira mnzake choipa; chotero chikondanocho chili chokwanitsa lamulo.
Explore AROMA 13:10
6
AROMA 13:7
Perekani kwa anthu onse mangawa ao; msonkho kwa eni ake a msonkho; kulipira kwa eni ake a kulipidwa; kuopa kwa eni ake a kuwaopa; ulemu kwa eni ake a ulemu.
Explore AROMA 13:7
Home
Bible
Plans
Videos